Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 9:36 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo pakutero mauwo, Yesu anapezedwa ali yekha. Ndipo iwo anakhala cete, ndipo sanauza munthu ali yense masiku aja kanthu konse ka izo anaziona.

Werengani mutu wathunthu Luka 9

Onani Luka 9:36 nkhani