Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 8:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo za m'mbali mwa njira ndiwo anthu amene adamva; pamenepo akudza mdierekezi, nacotsa mau m'mitima yao, kuti angakhulupirire ndi kupulumuka.

Werengani mutu wathunthu Luka 8

Onani Luka 8:12 nkhani