Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 7:44 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anati kwa iye, Waweruza bwino. Ndipo m'mene iye anaceukira kwa mkaziyo, anati kwa Simoni, Upenya mkazi ameneyu kodi? Ndinalowa m'nyumba yako, sunandipatsa madzi akusambitsa mapazi anga; koma uyu anakonkha mapazi anga ndi misozi, nawapukuta ndi tsitsi lace.

Werengani mutu wathunthu Luka 7

Onani Luka 7:44 nkhani