Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 7:40-43 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

40. Ndipo Yesu anayankha nati kwa iye, Simoni, ndiri ndi kanthu kakunena kwa iwe. Ndipo iye anabvomera, Mphunzitsi, nenani.

41. Munthu wokongoletsa ndalama anali nao amangawa awiri; mmodziyo anali ndi mangawa ace a marupiya mazana asanu, koma mnzace makumi asanu.

42. Popeza analibe cobwezera iwo, anawakhululukira onse awiri. Cotero, ndani wa iwo adzaposa kumkonda?

43. Simoni anayankha, nati, Ndiyesa kuti, iye amene anamkhululukira zoposa,

Werengani mutu wathunthu Luka 7