Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 5:36 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo iye ananenanso fanizo kwa iwo, kuti, Palibe munthu ang'amba cigamba ca maraya arsopano, naciphatika pa maraya akale; cifukwa ngati atero, angong'ambitsa atsopanowo, ndi cigamba ca atsopanowo sicidzayenerana ndi akalewo.

Werengani mutu wathunthu Luka 5

Onani Luka 5:36 nkhani