Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 5:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo iye analowa m'ngalawa imodzi, ndiyo yace ya Simoni, nampempha iye akankhe pang'ono. Ndipo anakhala pansi m'menemo, naphunzitsa m'ngalawa makamuwo a anthu.

Werengani mutu wathunthu Luka 5

Onani Luka 5:3 nkhani