Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 5:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo posapeza polowa naye, cifukwa ca unyinji wa anthu, anakwera pamwamba pa chindwi, namtsitsira iye poboola pa chindwi ndi kama wace, namfikitsa pakati pomwe pamaso pa Yesu.

Werengani mutu wathunthu Luka 5

Onani Luka 5:19 nkhani