Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 3:18-34 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

18. Coteretu iye anauza anthu Uthenga Wabwino ndi kuwadandaulira zinthu zina zambiri.

19. Koma Herode mfumu ija, m'mene Yohane anamdzudzula cifukwa ca Herodiya, mkazi wa mbale wace, ndi ca zinthu zonse zoina Herode anazicita,

20. anaonjeza pa zonsezi icinso, kuti anatsekera Yohane m'nyumba yandende.

21. Ndipo panali pamene anthu onse anabatizidwa, ndipo Yesu anabatizidwa, nalikupemphera, kuti panatseguka pathambo,

22. ndipo Mzimu Woyera anatsika ndi maonekedwe a thupi lace ngati nkhunda, nadza pa iye; ndipo munaturuka mau m'thambo, kuti, Iwe ndiwe Mwana wanga wokondedwa, mwa Iwe ndikondwera.

23. Ndipo Yesuyo, pamene anayamba nchito yace, anali monga wa zaka makumi atatu, ndiye (monga anthu adamuyesa) mwana wa Yosefe, mwana wa Heli,

24. mwana wa Matati, mwana wa Levi, mwana wa Melki, mwana wa Yanai, mwana wa Yosefe,

25. mwana wa Matatio, mwana wa Amosi, mwana wa Naumi, mwana wa Esli, mwana wa Nagai,

26. mwana wa Maati, mwana wa Matatio, mwana wa Semeini, mwana wa Yosefe, mwana wa Yoda,

27. mwana wa Yoanani, mwana wa Resa, mwana wa Zerubabeli, mwana wa Salatieli, mwana wa Neri,

28. mwana wa Melki, mwana wa Adi, mwana wa Kosamu, mwana wa Elmadama, rrrvana wa Ere,

29. mwana wa Jose, mwana wa Eliezere, mwana wa Yorimu, mwana wa Matati, mwana wa Levi,

30. mwana wa Simeoni, mwana wa Yuda, mwana wa Yosefe, mwana wa Yonamu, mwana wa Eliyakimu,

31. mwana wa Melea, mwana wa Mena, mwana wa Matata, mwana wa Natanu, mwana wa Davine,

32. mwana wa Jese, mwana wa Obede, mwana wa Boazi, mwana wa Salmoni, mwana wa Naasoni,

33. mwana wa Aminadabu, mwana wa Ami, mwana wa Ezronu, mwana wa Farese, mwana wa Yuda,

34. mwana wa Yakobo, mwana wa Isake, mwana wa Abrahamu, mwana wa Tera, mwana wa Nakoro,

Werengani mutu wathunthu Luka 3