Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 20:20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anamyang'anira, natumiza ozonda, amene anadzionetsera ngati olungama mtima, kuti akamkole pa mau ace, kotero kuti akampereke iye ku ukulu ndi ulamuliro wa kazembe.

Werengani mutu wathunthu Luka 20

Onani Luka 20:20 nkhani