Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 15:20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo iye ananyamuka, nadza kwa atate wace. Koma pakudza iye kutali, atate wace anamuona, nagwidwa cifundo, nathamanga, namkupatira pakhosi pace, nampsompsonetsa.

Werengani mutu wathunthu Luka 15

Onani Luka 15:20 nkhani