Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 14:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma pamene pali ponse waitanidwa iwe, pita nukhale pansi pa malo a kuthungo; kotero kuti pamene akadza iye anakuitana iwe, akanena ndi iwe, Bwenzi langa, sendera, kwera kuno; pomwepo udzakhala ndi ulemerero pamaso pa onse akuseama pacakudya pamodzi ndi iwe.

Werengani mutu wathunthu Luka 14

Onani Luka 14:10 nkhani