Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 11:1-3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ndipo kunali, pakukhala iye pamalo pena ndi kupemphera, m'mene analeka, wina wa ophunzira ace anati kwa iye, Ambuye, tiphunzitseni ife kupemphera, monganso Yohane anaphunzitsa ophunzira ace.

2. Ndipo anati kwa iwo, M'mene mupemphera nenani, Atate, Dzina lanu liyeretsedwe; Ufumu wanu udze;

3. tipatseni ife tsiku ndi tsiku cakudya ca patsiku.

Werengani mutu wathunthu Luka 11