Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 11:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kunali, pakukhala iye pamalo pena ndi kupemphera, m'mene analeka, wina wa ophunzira ace anati kwa iye, Ambuye, tiphunzitseni ife kupemphera, monganso Yohane anaphunzitsa ophunzira ace.

Werengani mutu wathunthu Luka 11

Onani Luka 11:1 nkhani