Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 1:20-22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

20. Ndipo taona, udzakhala wotonthola ndi wosakhoza kulankhula, kufikira tsiku limene zidzacitika izi, popeza kuti sunakhulupirira mau, anga, amene adzakwanitsidwa pa nyengo yace.

21. Ndipo anthu analikulindira Zakariya, nazizwa ndi kucedwa kwace m'kacisimo.

22. Koma m'mene iye anaturukamo, sanatha kulankhula nao; ndipo anazindikira kuti iye adaona masomphenya m'Kacisimo. Ndipo iye analinkukodola iwo, nakhalabe wosalankhula.

Werengani mutu wathunthu Luka 1