Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Cibvumbulutso 8:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anaomba mngelo wacitatu, ndipo idagwa kucokera kumwamba nyenyezi yaikuru, yoyaka ngati muuni, ndipo idagwa pa limodzi la magawo atatu a mitsinje, ndi pa akasupe amadzi;

Werengani mutu wathunthu Cibvumbulutso 8

Onani Cibvumbulutso 8:10 nkhani