Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Cibvumbulutso 14:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ndinapenya, taonani, mtambo woyera; ndi pamtambo padakhala wina monga Mwana wa munthu, wakukhala naye korona wagolidi pamutu pace, ndi m'dzanja lace zenga lakuthwa.

Werengani mutu wathunthu Cibvumbulutso 14

Onani Cibvumbulutso 14:14 nkhani