Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Cibvumbulutso 13:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo adzacilambira onse akukhala padziko, amene dzina lao silinalembedwa m'buku la moyo la Mwanawankhosa, wophedwa kuyambira makhazikidwe a dziko lapansi,

Werengani mutu wathunthu Cibvumbulutso 13

Onani Cibvumbulutso 13:8 nkhani