Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Cibvumbulutso 12:16-17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

16. Ndipo dziko linathandiza mkaziyo, ndi dziko linatsegula m'kamwa mwace, nilinameza madzi a mtsinje amene cinjoka cinalabvula m'kamwamwace.

17. Ndipo cinjoka cinakwiya ndi mkazi, nicinacoka kunka kucita nkhondondi otsala ambeu yace, amene asunga malamulo a Mulungu, nakhala nao umboni wa Yesu.

Werengani mutu wathunthu Cibvumbulutso 12