Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Cibvumbulutso 12:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ndinamva mau akuru m'Mwamba, nanena, Tsopano zafika cipulumutso, ndi mphamvu, ndi ufumu za Mulungu wathu, ndi ulamuliro wa Kristu wace; pakuti wagwetsedwa wonenera wa abale athu, wakuwanenera pamaso pa Mulungu wathu usana ndi usiku.

Werengani mutu wathunthu Cibvumbulutso 12

Onani Cibvumbulutso 12:10 nkhani