Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Cibvumbulutso 1:1-2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. CIBVUMBULUTSO ca Yesu Kristu, cimene Mulungu anambvumbulutsira acionetsere akapolo ace, ndico ca izi ziyenera kucitika posacedwa: ndipo potuma mwa mngelo wace anazindikiritsa izi kwa kapolo wace Yohane;

2. amene anacita umboni za mau a Mulungu, ndi za umboni wa Yesu Kristu, zonse zimene adaziona.

Werengani mutu wathunthu Cibvumbulutso 1