Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Aroma 4:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

monga kwalembedwa: Ndinakukhazika iwe kholo la mitundu yambiri ya anthu pamaso pa Mulungu amene iye anamkhulupirira, amene apatsa akufa moyo, ndi kuitana zinthu zoti palibe, monga ngati ziripo,

Werengani mutu wathunthu Aroma 4

Onani Aroma 4:17 nkhani