Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Akolose 2:19-22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

19. kucokera kwa iye amene thupi lonse, lothandizidwa ndi kulumikizidwa pamodzi mwa mfundo ndi mitsempa, likula ndi makulidwe a Mulungu.

20. Ngati munafa pamodzi ndi Kristu kusiyana nazo zoyambaza dziko lapansi, mugonieranii ku zoikikazo, monga ngati moyo wanu mukhala nao m'dziko lapansi,

21. usaikapo dzanja, usalawa, usakhudza,

22. (ndizo zonse zakuonongedwa pocita nazo), monga mwa malangizo ndi maphunziro a anthu?

Werengani mutu wathunthu Akolose 2