Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Akolose 2:18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Munthu ali yense asakunyengeni ndi kulanda mphotho yanu ndi kudzicepetsa mwini wace, ndikugwadira kwa angelo, ndi kukhalira mu izi adaziona, wodzitukumula cabe ndi zolingalira za thupi lace, wosagwiritsa mutuwo,

Werengani mutu wathunthu Akolose 2

Onani Akolose 2:18 nkhani