Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ahebri 7:24-27 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

24. koma iye cifukwa kuti akhala iye nthawi yosatha ali nao unsembe wosasinthika,

25. kucokera komwekoakhoza kupulumutsa konse konse iwo akuyandikira kwa Mulungu mwa iye, popeza ali nao moyo wace cikhalire wa kuwapembedzera iwo.

26. Pakuti mkulu wa ansembe wotere anatiyenera ife, woyera mtima, wopanda coipa, wosadetsedwa, wosiyana ndi ocimwa, wakukhala wopitirira miyamba;

27. amene alibe cifukwa ca kupereka nsembe tsiku ndi tsiku monga akulu a ansembe, yoyambira cifukwa ca zoipa za iwo eni, yinayi cifukwa ca zoipa za anthu; pakuti ici anacita kamodzi, kwatha, podzipereka yekha.

Werengani mutu wathunthu Ahebri 7