Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ahebri 4:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti mau a Mulungu ali amoyo, ndi ocitacita, ndi akuthwa koposa lupanga lakuthwa konse konse, napyoza kufikira kugawira moyo ndi mzimu, ndi zimfundo ndi mafuta a m'mafupa, nazindikiritsa zolingirira ndi zitsimikizo za mtima.

Werengani mutu wathunthu Ahebri 4

Onani Ahebri 4:12 nkhani