Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ahebri 2:16-18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

16. Pakuti ndithu salandira angelo, koma alandira mbeu ya Abrahamu.

17. Potero kudamuyenera kufanizidwa ndi abale m'zonse, kuti akadzakhala mkulu wa ansembe wadfundo ndi wokhulupirika m'zinthu zakwa Mulungu, kuti apereke dipo la zoipa za anthu.

18. Pakuti popeza adamva zowawa, poyesedwa yekha, akhoza kuthandiza iwo amene ayesedwa.

Werengani mutu wathunthu Ahebri 2