Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ahebri 10:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

mthunzi wa zokoma zirinkudza, osati cifaniziro ceni ceni ca zinthuzo, sicikhozatu, ndi nsembe zomwezi caka ndi caka, zimene azipereka kosalekeza, kuwayesera angwiro iwo akuyandikira.

Werengani mutu wathunthu Ahebri 10

Onani Ahebri 10:1 nkhani