Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

3 Yohane 1:8-11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

8. Cifukwa cace ife tiyenera kulandira otere, kuti tikakhale othandizana naco coonadi,

9. Ndalemba kanthu kwa Mpingo; komatu Diotrefe uja, wofuna kukhala wamkuru wa iwo, satilandira ife.

10. Momwemo, ndikadza ine, ndidzakumbutsa nchito zace zimene aeitazi, zakunena zopanda pace pa ife ndi mau oipa; ndipopopeza izi sizimkwanira, salandira abale iye yekha, ndipo ofuna kuwalandira awaletsa, nawataya kunja powaturutsa mu Mpingo,

11. Wokondedwa, usatsanza ciri coipa komatu cimene ciri cokoma. Iye wakucita cokoma acokera kwa Mulungu; ye wakucita coipa sanamuona Mulungu.

Werengani mutu wathunthu 3 Yohane 1