11. Pakuti iye wakumlankhula ayanjana nazo nchito zace zoipa.
12. Pokhala ndiri nazo zambiri zakukulemberani, sindifuna kucita ndi kalata ndi kapezi; koma ndiyembekeza kudza kwa inu, ndi kulankhula popenyana, kuti cimwemwecanucikwanire.
13. Akulankhulani ana a mbale wanu wosankhika.