Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Petro 2:21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti pakadakhala bwino kwa iwo akadakhala osazindikira njira ya cilungamo, ndi poizindikira, kubwerera kutaya lamulo lopatulika lopatsidwa kwa iwo.

Werengani mutu wathunthu 2 Petro 2

Onani 2 Petro 2:21 nkhani