Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Akorinto 5:6-9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

6. Pokhala nako kulimbika mtima nthawi zonse tsono, ndipo podziwa kuti pamene tiri kwathu m'thupi, sitiri kwa Ambuye,

7. (pakuti tiyendayenda mwa cikhulupiriro si mwa cionekedwe);

8. koma tilimbika mtima, ndipo tikondwera makamaka kusakhala m'thupi, ndi kukhala kwathu kwa Ambuye.

9. Cifukwa cacenso tifunitsitsa, kapena kwathu kapena kwina, kukhala akumkondweretsa iye.

Werengani mutu wathunthu 2 Akorinto 5