Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Yohane 3:1-2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Taonani, cikondico Atate watipatsa, kuti tichedwe ana a Mulungu; ndipo tiri ife otere. Mwa ici dziko lapansi silizindikira ife, popeza silimzindikira iye.

2. Okondedwa, tsopano riri ana a Mulungu, ndipo sicinaoneke cimene tidzakhala. Tidziwa kuti, pa kuoneka iye, tidzakhala ofanana ndi iye, Pakuti tidzamuona iye monga ali.

Werengani mutu wathunthu 1 Yohane 3