Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Timoteo 2:1-5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ndidandaulira tsono, poyambayamba, kuti acitike mapembedzo, mapemphero, mapembedzero, mayamiko, cifukwa ca anthu onse;

2. cifukwa ca mafumu ndi onse akucita ulamuliro kuti m'moyo mwathu tikakhale odika mtima, ndi acete m'kulemekeza Mulungu, ndi m'kulemekezeka monse.

3. Pakuti ici ncokoma ndi colandirika pamaso pa Mulungu Mpulumutsi wathu;

4. amene afuna anthu onse apulumuke, nafike pozindikira coonadi.

5. Pakuti pali Mulungu mmodzi, ndi Mtetezi mmodzi pakati pa Mulungu ndi anthu, ndiye munthu, Kristu Yesu,

Werengani mutu wathunthu 1 Timoteo 2