Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Atesalonika 2:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

koma tingakhale tidamva zowawa kale, ndipo anaticitira cipongwe, monga mudziwa, ku Filipi, tinalimbika pakamwa mwa Mulungu wathu kulankhula ndi inu Uthenga Wabwino wa Mulungu m'kutsutsana kwambiri.

Werengani mutu wathunthu 1 Atesalonika 2

Onani 1 Atesalonika 2:2 nkhani