Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Akorinto 8:9-11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

9. Koma yang'anirani kuti ulamuliro wanu umene ungakhale cokhumudwitsa ofokawo.

10. Pakuti wina akaona iwe amene uli naco cidziwitso, ulikukhala pacakudya m'kacisi wa fano, kodi cikumbu mtima cace, popeza ali wofoka, sieidzalimbika kudya zoperekedwa nsembe kwa mafano?

11. Pakuti mwa cidziwitso cako wofokayo atayika, ndiye mbale amene Kristu anamfera.

Werengani mutu wathunthu 1 Akorinto 8