Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Akorinto 8:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti wina akaona iwe amene uli naco cidziwitso, ulikukhala pacakudya m'kacisi wa fano, kodi cikumbu mtima cace, popeza ali wofoka, sieidzalimbika kudya zoperekedwa nsembe kwa mafano?

Werengani mutu wathunthu 1 Akorinto 8

Onani 1 Akorinto 8:10 nkhani