Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Akorinto 7:20-23 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

20. Yense akhale m'maitanidwe m'mene anaitanidwamo.

21. Kodi unaitanidwa uli kapolo? Usasamalako; koma ngati ukhozanso kukhala mfulu, cita nako ndiko.

22. Pakuti iye amene anaitanidwa mwa Ambuye, pokhala ali kapolo, ali mfulu ya Ambuye: momwemonso woitanidwayo, pokhala ali mfulu, ali kapolo wa Kristu.

23. Munagulidwa ndi mtengo wace; musakhale akapolo a anthu.

Werengani mutu wathunthu 1 Akorinto 7