Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Akorinto 4:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma izi, abale, ndadziphiphiritsira ndekha ndi Apolo, cifukwa ca inu, kuti mwa ife mukaphunzire kusapitirira zimene zilembedwa; kuti pasakhale mmodzi wodzitukumulira mnzace ndi kukana wina.

Werengani mutu wathunthu 1 Akorinto 4

Onani 1 Akorinto 4:6 nkhani