Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Akorinto 4:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa cace musaweruze kanthu isanadze nthawi yace, kufikira akadze Ambuye, amenenso adzaonetsera zobisika za mdima, nadzasonyeza zitsimikizo za mtima; ndipo pamenepo yense adzakhala nao uyamiko wace wa kwa Mulungu.

Werengani mutu wathunthu 1 Akorinto 4

Onani 1 Akorinto 4:5 nkhani