Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Akorinto 11:1-4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Khalani onditsanza ine, monga inenso oditsanza Kristu.

2. Ndipo ndikutamandani kuti m'zinthu zonse mukumbukila ine, ndi kuti musunga miyambo monga ndinapereka kwa inu.

3. Koma ndifunakuti mudziwe, kuti mutu wa munthu yense ndiye Kristu; ndi mutu wa mkazi ndiye mwamuna; ndipo mutu wa Kristu ndiye Mulungu,

4. Mwamuna yense wobveka mutu, popemphera kapena ponenera, anyoza mutu wace.

Werengani mutu wathunthu 1 Akorinto 11