Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Zekariya 8:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kudzacitika kuti, monga munali cotembereretsa mwa amitundu, inu nyumba ya Yuda, ndi nyumba ya Israyeli, momwemo ndidzakusungani, ndipo mudzakhala codalitsa naco; musaope, alimbike manja anu.

Werengani mutu wathunthu Zekariya 8

Onani Zekariya 8:13 nkhani