Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Zekariya 8:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti asanafike masiku aja, panalibe kulipidwira munthu, kapena kulipidwira nyama, ndipo analibe mtendere iye wakuturuka, kapena wakulowa, cifukwa ca wosautsa; pakuti ndinatumiza munthu yense atsutsane naye mnzace.

Werengani mutu wathunthu Zekariya 8

Onani Zekariya 8:10 nkhani