Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Zekariya 5:1-2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Pamenepo ndinakwezanso maso anga, ndinapenya, taonani, mpukutu wouluka.

2. Ndipo anati kwa ine, Uona ciani? Ndipo ndinayankha, Ndiona mpukutu wouluka; utali wace mikono makumi awiri, ndi citando cace mikono khumi.

Werengani mutu wathunthu Zekariya 5