Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Zekariya 2:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

nanena naye, Thamanga, lankhula ndi mnyamata uyu, ndi kuti, M'Yerusalemu mudzakhala anthu ngati m'midzi yopanda malinga, cifukwa ca kucuruka anthu ndi zoweta momwemo.

Werengani mutu wathunthu Zekariya 2

Onani Zekariya 2:4 nkhani