Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Zekariya 14:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kudzacitika kuti otsala onse a amitundu onse anadzawo kulimbana ndi Yerusalemu, adzakwera caka ndi caka kulambira mfumu Yehova wa makamu, ndi kusunga madyerero amisasa.

Werengani mutu wathunthu Zekariya 14

Onani Zekariya 14:16 nkhani