Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 8:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo Yehova anati kwa Yoswa, Usaope, kapena kutenga nkhawa, tenga anthu onse a nkhondo apite nawe, ndipo tauka, kwera ku Ai; taona, ndapereka m'dzanja lako mfumu ya ku Ai, ndi anthu ace ndi mudzi wace ndi dziko lace;

Werengani mutu wathunthu Yoswa 8

Onani Yoswa 8:1 nkhani