Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 6:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kudzakhala kuti akaliza cilizire ndi nyanga ya nkhosa yamphongo, nimumva kulira kwa mphalasa, anthu onse apfuule mpfuu yaikuru; ndipo linga la mudziwo lidzagwa pomwepo, ndi anthu adzakwera ndi kulowamo yense kumaso kwace.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 6

Onani Yoswa 6:5 nkhani