Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 6:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kunali, tsiku lacisanu ndi ciwiri analawira mamawa, mbandakuca, nazungulira mudzi mommuja kasanu ndi kawiri; koma tsiku lijalo anazungulira mudzi kasanu ndi kawiri.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 6

Onani Yoswa 6:15 nkhani