Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 3:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yehova anati kwa Yoswa, Lero lino ndidzayamba kukukuza pamaso pa Aisrayeli onse, kuti adziwe, kuti monga momwe ndinakhalira ndi Mose, momwemo ndidzakhala ndi iwe.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 3

Onani Yoswa 3:7 nkhani