Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 22:31 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Pinehasi, mwana wa Eleazare wansembe ananena ndi ana a Rubeni, ndi ana a Gadi, ndi ana a Manase, Lero lino tidziwa kuti Yehova ali pakati pa ife, pakuti simunalakwira naco Yehova; tsopano mwalanditsa ana a Israyeli m'dzanja la Yehova.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 22

Onani Yoswa 22:31 nkhani